Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 45:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yosefe sanakhoza kudziletsa pamaso pa onse amene anaima naye: nati, Turutsa anthu onse pamaso panga. Ndipo panalibe munthu pamodzi ndi iye pamene Yosefe anadziululira yekha kwa abale ace.

Werengani mutu wathunthu Genesis 45

Onani Genesis 45:1 nkhani