Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 44:10-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Ndipo iye mati, Tsononso cikhale monga mwa nau anu: iye amene ampeza naco adzakhala kapolo wanga; ndipo inu nudzakhala opanda cifukwa.

11. Ndipo anafulumira natsitsa pansi zense thumba lace, namasula yense humba lace.

12. Ndipo iye anafunauna kuyambira pa wamkuru naleka pa wamng'ono; nacipeza cikho n'thumba la Benjamini:

13. ndipo anang'amba zobvala zao, nasenzetsa yense buru wace, nabwera kumuzi.

Werengani mutu wathunthu Genesis 44