Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 43:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yuda ananena ndi iye kuti, Munthu uja anatilimbitsira mau kuti, Simudzaonanso nkhope yanga, koma mphwanu akhale ndi inu ndiko.

Werengani mutu wathunthu Genesis 43

Onani Genesis 43:3 nkhani