Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 43:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene anaona Benjamini pamodzi nao, anati kwa tsanyumba wace, Lowa nao anthuwo m'nyumba, kaphere iwo, kakoozere, cifukwa anthuwo adzadya ndi ine usana uno.

Werengani mutu wathunthu Genesis 43

Onani Genesis 43:16 nkhani