Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 42:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Rubeni anayankha nati kwa iwo, Kodi sindinanena kwa inu kuti, Musacimwire mwanayu; ndipo inu munakana kumvera? cifukwa cacenso, taonani mwazi wace ufunidwa.

Werengani mutu wathunthu Genesis 42

Onani Genesis 42:22 nkhani