Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 41:51 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yosefe anamucha dzina la woyamba Manase, cifukwa anati iye, Mulungu wandiiwalitsa ine zobvuta zanga zonse, ndi nyumba yonse ya atate wanga.

Werengani mutu wathunthu Genesis 41

Onani Genesis 41:51 nkhani