Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 40:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo panali zitapita izi, wopereka cikho wa mfumu ya Aigupto ndi wophika mkate wace anamcimwira mbuye wao mfumu ya Aigupto.

2. Ndipo Farao anakwiyira akuru ace awiriwo wamkuru wa opereka cikho, ndi wamkuru wa ophika mkate.

3. Ndipo anaika iwo asungidwe m'nyumba ya kazembe wa alonda, m'kaidi, umo anamangidwa Yosefe.

Werengani mutu wathunthu Genesis 40