Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 38:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye anapatukira kwa mkazi panjira, nati, Tiyetu, ndilowane nawe; cifukwa sanamdziwa kuti ndiye mpongozi wace. Ndipo anati, Kodi udzandipatsa ine ciani kuti ulowane ndi ine.

Werengani mutu wathunthu Genesis 38

Onani Genesis 38:16 nkhani