Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 38:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anabvula zobvala zacezamasiye, nadzipfundandi copfunda cace, nabvala nakhala pa cipata ca Enaimu, cifukwa ciri pa njira ya ku Timna; pakuti anaona kuti Sela anakula msinkhu, ndipo sanampatsa iye kuti akhale mkazi wace.

Werengani mutu wathunthu Genesis 38

Onani Genesis 38:14 nkhani