Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 37:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

natumiza malaya amwinjiro, nadza nao kwa atate ao: ndipo anati, Siwa tawatola; muzindikire tsono ngati ndi malaya a mwana wanu, kapena ndi ena.

Werengani mutu wathunthu Genesis 37

Onani Genesis 37:32 nkhani