25. Ana a Ana ndi awa: Disoni ndi Oholibama mwana wamkazi wa Ana.
26. Ana a Disoni ndi awa: Hemadani ndi Esibani ndi Itirani, ndi Kerana.
27. Ana a Ezeri ndi awa: Biliha, ndi Zavani, ndi Akani.
28. Ana a Disoni ndi awa: Uzi ndi Arana.
29. Mafumu obadwa kwa Ahori: mfumu Lotani, mfumu Sobali, mfumu Zibeoni, mfumu Ana,
30. mfumu Disoni, mfumu Ezeri, mfumu Disani; amenewa ndi mafumu obadwa kwa Ahori, monga mwa maufumu ao m'dziko la Seiri.