Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 36:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Amenewa ndi ana amuna a Reueli mwana wamwamuna wa Esau: mfumu Nahati, mfumu Zera, mfumu Sama, mfumu Miza; amenewa ndi mafumu obadwa kwa Reueli m'dziko la Edomu: amenewa ndi ana amuna a Basemati mkazi wace wa Esau.

Werengani mutu wathunthu Genesis 36

Onani Genesis 36:17 nkhani