Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 35:28-29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Ndipo masiku a Isake anali zaka zana limodzi kudza makumi asanu ndi atatu.

29. Ndipo Isake anatsirizika nafa, nasonkhanitsidwa kwa anthu a mtundu wace, wokalamba ndi wa masiku okwanira: ndipo Esau ndi Yakobo ana ace amuna anamuika iye.

Werengani mutu wathunthu Genesis 35