Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 34:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamva Yakobo kuti anamuipitsa Dina, mwana wace wamkazi; ana ace amuna anali ndi zoweta zace kudambo: ndipo Yakobo anakhala cete mpaka anafika iwo.

Werengani mutu wathunthu Genesis 34

Onani Genesis 34:5 nkhani