Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 34:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali tsiku lacitatu pamene anamva kuwawa, ana amuna awiri a Yakobo, Simeoni ndi Levi, abale ace a Dina, anatenga wina lupanga lace wina lace, nalimbika mtima nalowa m'mudzi napha amuna onse.

Werengani mutu wathunthu Genesis 34

Onani Genesis 34:25 nkhani