Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 32:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ngamila zamkaka makumi atatu ndi ana ao, ng'ombe zazikazi makumi anai, zazimuna khumi, aburu akazi makumi awiri ndi ana khumi.

Werengani mutu wathunthu Genesis 32

Onani Genesis 32:15 nkhani