Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 31:43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Labani anayankha nati kwa Yakobo, Akaziwa ndiwo ana anga, anawa ndiwo ana anga, zowetazi ndizo zoweta zanga ndi zonse ulinkuziona ndizo zanga: nanga ndidzacitira ine ciani lero kwa ana anga akazi amenewa, kapena ana ao amene anabala?

Werengani mutu wathunthu Genesis 31

Onani Genesis 31:43 nkhani