Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 31:41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndinakhala cotere zaka makumi awiri m'nyumba mwako; zaka khumi ndi zinai ndinakutumikira iwe cifukwa ca ana ako akazi awiri, ndi zaka zisanu ndi cimodzi cifukwa ca zoweta zako; wasintha malipiro anga kakhumi.

Werengani mutu wathunthu Genesis 31

Onani Genesis 31:41 nkhani