Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 31:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Rakele anati kwa atate wace, Asakwiye mbuyanga kuti sindingathe kuuka pamaso panu; cifukwa zocitika pa akazi ziri pa ine. Ndipo Labani anafunafuna koma sanapeze aterafiwo.

Werengani mutu wathunthu Genesis 31

Onani Genesis 31:35 nkhani