Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 3:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene anaona mkaziyo kuti mtengo unali wabwino kudya, ndi kuti unali wokoma m'maso, mtengo wolakalakika wakupatsa nzeru, anatenga zipatso zace, nadya, napatsanso mwamuna wace amene ali nave, nadya iyenso,

Werengani mutu wathunthu Genesis 3

Onani Genesis 3:6 nkhani