Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 29:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yakobo anamtumikira zaka zisanu ndi ziwiri cifukwa ca Rakele; koma zidamuonekera iye ngati masiku owerengeka cifukwa ca cikondi cimene anamkonda iye naco.

Werengani mutu wathunthu Genesis 29

Onani Genesis 29:20 nkhani