Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 29:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Labani anati kwa Yakobo, Cifukwa iwe ndiwe mbale wanga, kodi udzanditumikira ine kwacabe? Undiuze ine, malipiro ako adzakhala otani?

Werengani mutu wathunthu Genesis 29

Onani Genesis 29:15 nkhani