Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 29:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali pamene Labani anamva mbiri ya Yakobo mwana wa mlongo wace, iye anathamangira kukakomana naye namfungatira, nampsompsona, namlowetsa m'nyumba mwace. Ndipo iye anamfotokozera Labani zinthu zonsezo.

Werengani mutu wathunthu Genesis 29

Onani Genesis 29:13 nkhani