Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 28:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anafika kumalo, nagona kumeneko usiku, cifukwa lidalowa dzuwa: ndipo anatenga mwala wa kumeneko, nauika pansi pa mutu wace, nagona tulo kumeneko.

Werengani mutu wathunthu Genesis 28

Onani Genesis 28:11 nkhani