Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 25:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma kwa ana a akazi ace ang'ono amene Abrahamu anali nao Abrahamu anapatsa mphatso, nawacotsa iwo kwa Isake mwana wace, akali ndi moyo, kuti anke kum'mawa, ku dziko la kum'mawa.

Werengani mutu wathunthu Genesis 25

Onani Genesis 25:6 nkhani