Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 25:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Zaka za moyo wa Ismayeli ndi izi: zaka zana limodzi kudza makumi atatu ndi zisanu ndi ziwiri: ndipo iye anamwalira, natengedwa akhale ndi a mtundu wace.

Werengani mutu wathunthu Genesis 25

Onani Genesis 25:17 nkhani