Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 24:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova Mulungu wa Kumwamba, amene ananditenga ine ku nyumba ya atate wanga, ku dziko la abale anga, amene ananena ndi ine, amene analumbirira ine kuti, Ndidzapatsa mbeu zako dziko ili; iye adzatumiza mthenga wace akutsogolere, ndipo udzamtengere mwana wanga mkazi kumeneko.

Werengani mutu wathunthu Genesis 24

Onani Genesis 24:7 nkhani