Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 24:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo ndidzakulumbiritsa iwe pa Yehova, Mulungu wa Kumwamba, ndi Mulungu wa dziko lapansi, kuti usadzamtengere mwana wanga mkazi wa kwa ana akazi a Akananiwo, amene ndikhala pakati pao.

Werengani mutu wathunthu Genesis 24

Onani Genesis 24:3 nkhani