Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 24:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali, asanathe kunena, taonani, anaturuka Rebeka, amene anambala Betuele, mwana wamwamuna wa Milika, mkazi wa Nahori mphwace wa Abrahamu, ndi mtsuko wace paphewa pace.

Werengani mutu wathunthu Genesis 24

Onani Genesis 24:15 nkhani