Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 20:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Abimeleke anaitana Abrahamu, nati kwa iye, Waticitira ife ciani iwe? Ndakucimwiranji iwe kuti waufikitsa pa ine ndi pa ufumu wanga ucimo waukuru? Wandicitira ine zosayenera kuzicita.

Werengani mutu wathunthu Genesis 20

Onani Genesis 20:9 nkhani