Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 20:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsopano, umbwezere munthuyo mkazi wace; cifukwa iye ndiye mneneri, ndipo adzakupempherera iwe, ndipo udzakhala ndi moyo: koma ukaleka kumbwezera, udziwe kuti udzafa ndithu, iwe ndi onse amene uli nao.

Werengani mutu wathunthu Genesis 20

Onani Genesis 20:7 nkhani