Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 20:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali pamene Mulungu anandiyendetsa ine kunyumba kwa atate wanga, ndinati kwa mkaziyo, Ici ndico cokoma mtima udzandicitire ine, konse kumene tidzafika ife, uzinena za ine, iye ndiye mlongo wanga.

Werengani mutu wathunthu Genesis 20

Onani Genesis 20:13 nkhani