Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 18:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati, Ndidzabwera kwa iwe ndithu pakufika nyengo yace; taonani Sara mkazi wako adzakhala ndi mwana wamwamuna. Ndipo Sara anamva pakhomo pa hema amene anali pambuyo pace.

Werengani mutu wathunthu Genesis 18

Onani Genesis 18:10 nkhani