Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 16:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati, Hagara, mdzakazi wace wa Sarai, ufumira kuti? Unka kuti? Ndipo anati, Ndithawa ine kumaso kwace kwa wakuka wanga Sarai.

Werengani mutu wathunthu Genesis 16

Onani Genesis 16:8 nkhani