Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 15:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamturutsa iye kunja, nati, Tayang'anatu kumwamba, uwerenge nyenyezi, ngati ukhoza kuziwerenga zimenezo: ndipo anati kwa iye, Zoterezo zidzakhala mbeuzako.

Werengani mutu wathunthu Genesis 15

Onani Genesis 15:5 nkhani