Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 15:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsiku lomwelo Yehova anapangana cipangano ndi Abramu, nati, Ndidzapatsa mbeu zako dziko ili, kuyambira pa nyanja ya Aigupto kufikira pa nyanja yaikuru, nyanja ya Firate:

Werengani mutu wathunthu Genesis 15

Onani Genesis 15:18 nkhani