Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 10:29-32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

29. ndi Ofiri ndi Havila, ndi obabi; onse amenewa ndi ana a okitani.

30. Kwao kunayamba pa Mesa pakunka ku Sefere phiri la kum'mawa.

31. Amenewa ndi ana a Semu, monga mwa mabanja ao, mwa zinenedwe zao, m'maiko ao, m'mitundu yao.

32. Amenewo ndi mabanja a ana a Nowa monga mwa mibadwo yao, m'mitundu yao: ndi amenewo anagawanika mitundu pa dziko lapansi, citapita cigumula.

Werengani mutu wathunthu Genesis 10