Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 10:13-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. Mizraimu ndipo anabala Ludimu, ndi Anamimu, ndi Lehabimu, ndi Nafituhimu,

14. ndi Patrusimu, ndi Kasiluhimu, m'menemo ndipo anaturuka Afilisti, ndi Kafitorimu.

15. Ndipo Kanani anabala Sidoni woyamba wace, ndi Heti:

16. ndi Ajebusi, ndi Aamori, ndi Agirigasi;

17. ndi Ahivi, ndi Aariki, ndi Asini;

18. ndi Aaravadi, ndi Aazemari, ndi Ahamati; pambuyo pace pamenepo ndipo mabanja a Akanani anafalikira.

19. Ndipo malire a Akanani anayamba pa Sidoni, pakunka ku Gerari ndi ku Gaza; pakunka ku Sodomu, ndi ku Gomora, ndi Adima, ndi Zeboimu, kufikira ku Lasa.

20. Amenewa ndi ana amuna a Hamu monga mwa mabanja ao, mwa zinenedwe zao, m'maiko ao, m'mitundu yao.

Werengani mutu wathunthu Genesis 10