Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 8:7-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Ndipo anadza nane ku cipata ca kubwalo, ndipo popenya ine, taonani, pobooka palinga.

8. Pamenepo anati kwa ine, Wobadwa ndi munthu iwe, booletsa kulinga; ndipo nditabooletsa palinga, ndinaona khomo.

9. Ndipo anati kwa ine, Lowa, kapenye zonyansa zoipa alikuzicita komweko.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 8