Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 7:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace ndidzabwera nao amitundu oipitsitsa, ndipo iwo adzalandira nyumba zao ngati colowa, ndidzaleketsanso kudzikuza kwa amphamvu, kuti adetsedwe malo ao opatulika.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 7

Onani Ezekieli 7:24 nkhani