Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 45:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo dziko lace la mudziwo mulipereke la zikwi zisanu kupingasa kwace, ndi zikwi makumi awiri mphambu zisanu m'litali mwace, pa mbali ya cipereko copatulika, ndilo la nyumba yonse ya Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 45

Onani Ezekieli 45:6 nkhani