Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 44:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma adzakhala atumiki m'malo anga opatulika, akuyang'anira ku zipata za kacisi, ndi kutumikira m'kacisimo, aziwaphera anthu nsembe yopsereza, ndi nsembe yophera naime pamaso pao kuwatumikira.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 44

Onani Ezekieli 44:11 nkhani