Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 43:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo maonekedwe a masomphenya ndinawaona anali monga masomphenya aja ndinawaona pakudza ine kupasula mudzi; ndi masomphenyawa anali ngati masomphenya aja ndinawaona ku mtsinje wa Kebara; ndipo ndinagwa nkhope pansi.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 43

Onani Ezekieli 43:3 nkhani