Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 41:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Momwemo anayesa m'litali mwace nyumbayo inali kutsogolo kwace kwa mpata wokhala cakuno cace, ndi makonde ace am'mwamba, cakuno ndi cauko, mikono zana limodzi, ndi Kacisi wa m'katimo, ndi makonde a kubwalo;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 41

Onani Ezekieli 41:15 nkhani