Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 40:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi zipinda zace ndizo zitatu cakuno, ndi zitatu cauko, ndi makhoma a pakati pace; ndi zidundumwa zace zinali monga mwa muyeso wa cipata coyambaco, m'litali mwace mikono makumi asanu, ndi kupingasa kwace mikono makumi awiri mphambu isanu.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 40

Onani Ezekieli 40:21 nkhani