Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 39:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adzasenza manyazi ao, ndi zolakwa zao zonse, zimene anandilakwira nazo, pokhala mosatekeseka iwo m'dziko lao, opanda wina wakuwaopsa;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 39

Onani Ezekieli 39:26 nkhani