Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 34:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nkhosa zanga zinasokera ku mapiri ali onse, ndi pa citunda ciri conse cacitali; inde nkhosa zanga zinabalalika pa dziko lonse lapansi, ndipo panalibe wakuzipwaira kapena kuzifunafuna.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 34

Onani Ezekieli 34:6 nkhani