Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 33:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wobadwa ndi munthu iwe, Nena ndi ana a anthu a mtundu wako, uziti nao, Ndikafikitsira dziko liri lonse lupanga, nakatenga eni dziko munthu wa pakati pao, nakamuika awadikirire,

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 33

Onani Ezekieli 33:2 nkhani