Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 32:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Akalonga a kumpoto ali komwe onsewo, ndi Azidoni onse, amene anatsikira pamodzi ndi ophedwa, nacita manyazi cifukwa ca kuopsetsa anacititsaku ndi mphamvu yao, nagona osadulidwa pamodzi ndi iwo ophedwa ndi lupanga, nasenza manyazi ao pamodzi ndi iwo otsikira kudzenje.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 32

Onani Ezekieli 32:30 nkhani