Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 32:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wobadwa ndi munthu iwe, takwezera Farao mfumu ya Aigupto nyimbo yamaliro; uziti naye, Unafanana nao msona wa mkango wa amitundu, unanga ng'ona ya m'nyanja, unabuka m'mitsinje mwako, nubvundulira madzi ndi mapazi ako, ndi kudetsa mitsinje yao.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 32

Onani Ezekieli 32:2 nkhani